Polankhula la chiwiri pa Chilumba cha Chizumulu pamwambo otsegulira ofesiyi omwe unatsogozedwa ndi Phungu wa Likoma a Christopher Ashems Songwe, ndunayi yati …
April 2025
-
-
Sports
Team ya Chiponde FC ndi akatswiri a FAM Cup Under 21 District League itagonjetsa Team ya Red Arrows 4-2.
Masewero omwe anachitikira pa Likoma Community Football ground la lamulungu anabweletsa kwimbi la anthu kuchokera m’madera onse aboma la Likoma ndipo anali …
-
Featured
Khonsolo ya Likoma yati mwayi wa ntchito zosiyanasiyana ulipo mukhonsoloyi kwa achinyamata omwe ali ndi zowayeneleza.
Poyankha funso la phungu wa Likoma a Christopher Ashems Songwe lomwe anafunsa lachisanu pa mkumano wa Full Council lokhudza ndondomeko zakalembedwe ka …
-
Politics
Phungu waboma la Likoma a Christopher Ashems Songwe wati pali zokhoma zina zomwe zachititsa kuti munthawi yawo asakwanitse zina mwa zitukuko zomwe adalonjaza.
A Songwe anena izi lolemba pomwe anakonza mkumano wa adindo osiyanasiyana kuphatikizapo mafumu ndicholinga chowafotokozera zomwe achita kuchokera mchaka cha 2019. “Munthawi …
-
Lifestyle
Anthu okhala pa Chilumba cha Chizumulu apempha Boma kuti lipitilize mapulani omanga Jiti pachilumbachi.
Izi zadziwika pa mkumano omwe phungu wanyumba ya malamulo wa Likoma a Christopher Ashems Songwe anayitanitsa adindo osiyanasiyana kuphatikizapo mafumu lero pomwe …
-
Lifestyle
Ngati njira imodzi yochepetsa umbanda m’boma la Likoma Senior Chief Mkumpha yachititsa mkumano wa asodzi ochokela m’ma boma ena.
Polankhula pamsonkhanowu a Mathews Mwela anati anayitanitsa mkumanowu pomwe asodzi ochokera m’maboma ena akupita ku Likoma kukachita usodzi komanso bizinesi, asodziwa akuchokela …
-
Featured
Nthambi yowona zanyengo ndi kusintha kwa nyengo yati mitambo ya mvula ya mabingu yayambapo kale kusonkhana m’madera ena am’dziko muno.
Madelawa ndi monga, Blantyre, Thyolo, Phalombe, Mangochi, Mwanza, Salima mwa ochepa chabe. Nthambiyi yati izi zikupereka chiyembekezo cha mvula ya mabingu m’maderawa …
-
Featured
Apolice M’boma la Likoma agwira abambo atatu ndikuwasunga muchitolokosi powaganizira mulandu wakuba komanso kupezeka ndi katundu wa anthu omwe anamira pangozi ya bwato yomwe inachitika loweluka sabata yapitayi m’bomali pomwe anthuwa amakakwera sitima ya MV Chilembwe.
Malingana ndi ofalitsa nkhani za Police ku Likoma sergeant Enala Kaluwa wati pawukadaulo wawo akwanitsa kugwira anthuwa ndipo onsewa akuyembekezeka kukawonekera kubwalo …
-
Featured
Sitima ya MV Chilembwe idziyenda kawiri patsiku kuyambila pa 15 April pakati pa boma la Likoma ndi Nkhata Bay.
“Ndiyankha pompano zokhudza MV Chilembwe zomwe phungu wanyumba ya malamulo wapempha”, nduna yowona za mayendedwe ndi mtengatenga a Jacob Hara ndiwo anena …
-
Featured
Opindula ndi ndondomeko ya mtukula pakhomo m’boma la Likoma ati njira yatsopano yolandila ndalama kudzera pa phone ndiyodalilika.
Izi zadziwika Likoma radio itayendera ena mwa opindula ndi ndondomekoyi pa chilumba cha Chizumulu kufuna kunva momwe opindulawa ayilandilila njila yamakonoyi yomwe …