Phunguyu wapeleka thandizo la ndalama zokwana 1,000,000.00-kwacha lachisanu kudzera ku ofesi ya za masewero, District Education Sports Officer (DESO). Polandila thandizoli mkulu …
May 2025
-
-
Politics
Gulu la Taskforce lomwe ndi nthambi ya chipani cha Malawi Congress Party m’boma la Likoma lapeleka Cement kuti amalizile nyumba ya chigayo.
Polankhula lachinayi pamwambo opeleka cement ku komiti yoyendetsa chigayochi, a Innocent Aponda omwe ndi mmodzi mwa guluri ati achita chidwi powona momwe …
-
Lifestyle
Wapampando wa khonsolo ya boma la Likoma wati anthu omwe amapindula ndi porogalamu ya mtukula pakhomo adzigwilitsa moyenera ndalama zomwe amalandila mu porogalamuyi.
A Barnabas Sambamu anena izi lamulungu pomwe khonsolo ya Likoma inakonza masewelo ampira wamiyendo ndicholinga chakuti apeleke uthenga wamomwe porogalamuyi imayendela, pamutu …
-
Lifestyle
Gulu la Tilerane la m’mudzi wa mfumu Mani M’boma la Likoma lathandiza mabanja awiri osowa ndikatundu ogonera.
Polankhula loweluka pamwambo opeleka katundu kumabanjawa, Wapampando wa Guluri mayi Gladies Njakale ati cholinga chaguluri ndikuonetsetsa kuti anthu akukhala moyo wopanda nkhawa, …
-
Featured
Pomwe dziko lino likukonzekera chisankho chapatatu bungwe loyendetsa chisankho la Malawi Electral Commission likupitiliza kudziwitsa adindo osiyanasiyana za ndondomeko yachisankho.
Mkulu owona zachisankho m’boma la Likoma a Theophilus Msachi lero achititsa mkumano wa mafumu ndi atsogoleli azipembedzo pofuna kuwadziwitsa za ntchito yotsimikizila …
-
Featured
Mulandu wayemwe akumuganizira kuti ndi m’modzi mwawoyendetsa Boat lomwe linachita ngozi ndikupha anthu nkhumi ndi modzi m’mawa wapa 12 April, 2025, m’boma la Likoma wayamba lero.
Malingana ndi His Worship Fordwatch Nyamazana Mkandawire wati mlanduwu ukuyembekezeka kupitilira lachisanu sabata ino. Naye otengera milandu ku bwalo lamilandu Sergeant Charles …
-
Lifestyle
Chiponde Beach Resort yakonza mwambo wapadera pofuna kubweletsa pamodzi anthu ochita malonda m’boma la Likoma.
M’mawu ake mkulu wamalo ogona alendo a Chiponde Beach Resort a Gedion Khuni ati mwambowu ubweletsa pamodzi anthu ochita malonda osiyanasiyana kuphatikizapo …
-
Nthambi yowona zanyengo ndi kusintha kwanyengo yati nyengo ya Chiperoni ikuyembekezeka kuchepa mphanvu lero ndipo mawa m’madera ambiri kudzakhala kwa nyengo ya …