Izi zili chonchi kutsatila masewero omwe anachitika Lamulungu lapitali pa Madimba Community Ground mndime ya Semi final pakati pa Nkhwazi fc ndi …
Monthly Archives
September 2025
-
-
Featured
‎kutsatila kutsegulira kwa sukulu pa 22 September chaka chino, gulu la achinyamata lochokera kwa a mfumu a Mani m’mudzi wa Mbungo lapeleka makope ndi zolembera kwa ana apasukulu ya mbungo m’boma la Likoma.‎‎
M,modzi mwa achinyamata omwe apelereka makopewa a Nick Mkuyamba ati cholinga chachikulu cha gulu lawo ndikupititsa patsogolo maphunziro musukulu za primary m’bomali.‎‎Nawo …
-
Vuto lakusowa kwa madzi a ukhondo lafika posauzana pa chilumba cha chizumulu m’boma la Likoma. Polankhula ndi Likoma Radio mkulu woyang’anira sikimu …