Home Lifestyle Anthu okhala pa Chilumba cha Chizumulu apempha Boma kuti lipitilize mapulani omanga Jiti pachilumbachi.

Anthu okhala pa Chilumba cha Chizumulu apempha Boma kuti lipitilize mapulani omanga Jiti pachilumbachi.

by Oliver Malibisa
0 comments

Izi zadziwika pa mkumano omwe phungu wanyumba ya malamulo wa Likoma a Christopher Ashems Songwe anayitanitsa adindo osiyanasiyana kuphatikizapo mafumu lero pomwe amapeleka malipoti ake amomwe ntchito za chitukuko zayendera m’bomali kuyambila chaka cha 2019 mpaka 2025.

T.A Kabuthu wa chilumba cha Chizumulu wati zosemphana zomwe zinalipo zokhudza malo omwe jitiyi idzamangidwe zatha tsopano.

Enala Phiri yemwe ndi ochita malonda pa chilumbachi wati amayi ndi achikulire ndiwomwe akuvutika pokwera Sitima ndipo ndipo wati ganizo lopitiliza ntchitoyi ndiyopindulira anthu apachilumbachi

Naye wachinyamata ochokera m’dera la Chiteko pachilumbachi macfallen Mafuta ati ndizoona kuti pakali pano kusemphanaku kunatha ndipo boma lipitilize ndi ganizoli.

LikomaFM, online news.

You may also like

Leave a Comment

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00