A Chilambula anena izi lamulungu kutsatila kufika kwa incinerator yi pa chipatala cha Chima m’bomali. “Kumbuyoku tikafuna kuwotcha zinthu zina tinkazitumiza ku …
Chiletso Bisweck
-
-
Featured
Ofesi yowona za usodzi ku Likoma yati ndiyokondwa kuti tsopano asodzi ali ndi owaimira ku khonsolo.
Mkulu woyendetsa ntchito za usodzi m’boma la Likoma, Lonjezo Chikopa wati tsopano pakhala posavuta kuti asodzi azitha kutula nkhawa zawo komanso kudziwa …
-
Featured
Wapampando oyang’anila chitukuko chadera la kumwera kwa chilumba cha Likoma a Anson Putaputa ati akusowekera maphunziro kuti ayambe kugwira ntchito yawo mwaukadaulo.
A Putaputa anena izi kutsatila zomwe wachiwiri kwa nduna yoona za umoyo yemwenso ndi phungu wa boma la Likoma a Charles Chilambula …
-
Featured
Wachiwiri kwa nduna ya zaumoyo yemwenso ndi phungu wa Likoma Islands Constituency olemekezeka a Charles Broomhead Chilambula ati boma ndilodzipereka kupititsa patsogolo ntchito zaumoyo.
A Chilambula amalankhula izi lero pamwambo otsegulira chipatala chaching’ono cha YoMa chomwe chamangidwa m’mudzi wa Yofu m’boma la Likoma. A Chilambula ati …
-
Entertainment
Atachita zii kwa zaka zinayi m’modzi mwa oyimba wapa chilumba cha Chizumulu, Memory Pondomali yemwe amatchuka ndi dzina lakuti Nyapondo wati akhala akutulutsa nyimbo yatsopano yomwe akuyitcha “Zani”.
Nyapondo wati nyimboyi yomwe wajambula Video komanso audio zonse zitulutsidwa pa 1 February 2026, “panopa ndikhala okhazikika chifukwa ndinawoloka zomwe zakhala zikundifowoketsa …
-
Featured
Khonsolo ya Likoma yalandira ma Computer asanu othandizira sukulu ya Likoma community technical college kuchokera ku Bungwe la TEVETA.
Polankhula lolemba pamwambo opeleka ma computer wa, mkulu woyendetsa ntchito za TEVETA m’chigawo chakumpoto a Joseph Chikopa ati ndicholinga chawo kuti Likoma …
-
Featured
Khansala Justina Phiri wa chigawo chakumpoto kwa Chilumba cha Chizumulu ndiyemwe wasankhidwa kukhala Wapampando wa Khonsolo ya Likoma.
Pa chisankho chomwe chachitika Lolemba motsogozedwa ndi bwana mkubwa wa khonsolo ya Likoma Abubakar Nkhoma, a Justina Phiri agonjetsa a Enerst Gulu …
-
Lifestyle
Mwiniwake wa malo ogona alendo omwe akuwatcha kuti Mwayi Wanga Guest House m’boma la Likoma ati malowa awatsegulira pa 12 mwezi uno.
A Yamikani Mwambafula awuza Likoma Radio kuti pakadali pano chilichonse chokonzekera mwambowu chilimchimake ndipo ati patsikuli anthu ayembekezere kudzasangalatsidwa ndi oyimba osiyanasiyana …
-
Sports
Team ya Try Again FC yafika mu ndime yotsiliza mu chikho cha Castel Challenge Cup itagonjetsa Nkhwazi FC 2 kwa du.
Izi zili chonchi kutsatila masewero omwe anachitika Lamulungu lapitali pa Madimba Community Ground mndime ya Semi final pakati pa Nkhwazi fc ndi …
-
Featured
‎kutsatila kutsegulira kwa sukulu pa 22 September chaka chino, gulu la achinyamata lochokera kwa a mfumu a Mani m’mudzi wa Mbungo lapeleka makope ndi zolembera kwa ana apasukulu ya mbungo m’boma la Likoma.‎‎
M,modzi mwa achinyamata omwe apelereka makopewa a Nick Mkuyamba ati cholinga chachikulu cha gulu lawo ndikupititsa patsogolo maphunziro musukulu za primary m’bomali.‎‎Nawo …