Polankhula pamsonkhanowu a Mathews Mwela anati anayitanitsa mkumanowu pomwe asodzi ochokera m’maboma ena akupita ku Likoma kukachita usodzi komanso bizinesi, asodziwa akuchokela …
Author
Chiletso Bisweck
-
-
Featured
Nthambi yowona zanyengo ndi kusintha kwa nyengo yati mitambo ya mvula ya mabingu yayambapo kale kusonkhana m’madera ena am’dziko muno.
Madelawa ndi monga, Blantyre, Thyolo, Phalombe, Mangochi, Mwanza, Salima mwa ochepa chabe. Nthambiyi yati izi zikupereka chiyembekezo cha mvula ya mabingu m’maderawa …
-
Featured
Opindula ndi ndondomeko ya mtukula pakhomo m’boma la Likoma ati njira yatsopano yolandila ndalama kudzera pa phone ndiyodalilika.
Izi zadziwika Likoma radio itayendera ena mwa opindula ndi ndondomekoyi pa chilumba cha Chizumulu kufuna kunva momwe opindulawa ayilandilila njila yamakonoyi yomwe …
Older Posts