Home Lifestyle Chiponde Beach Resort yakonza mwambo wapadera pofuna kubweletsa pamodzi anthu ochita malonda m’boma la Likoma.

Chiponde Beach Resort yakonza mwambo wapadera pofuna kubweletsa pamodzi anthu ochita malonda m’boma la Likoma.

by Oliver Malibisa
0 comments

M’mawu ake mkulu wamalo ogona alendo a Chiponde Beach Resort a Gedion Khuni ati mwambowu ubweletsa pamodzi anthu ochita malonda osiyanasiyana kuphatikizapo mbeu zomwe zimalimadwa m’bomali.

Iwo atinso pamwambowu padzakakhala kupeleka mphoto komanso kugulitsa zinthu zosiyanasiyana monga tomato, masamba, chinangwa komanso malonda ena pamitengo yotsika kusiyana ndi momwe zimagulitsidwira nthawi zonse.

Mwambo omwe akuutcha kuti Farmers Market, udzachitika pa 1 June 2025, ndipo ukachitikira ku Chiponde Beach Resort pomwe oyimba osiyanasiyana akakometsele mwambowu motsogodzedwa ndi Limban Band.

LikomaFM, OnlineNews.

You may also like

Leave a Comment

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00