Home Lifestyle Gulu la Tilerane la m’mudzi wa mfumu Mani M’boma la Likoma lathandiza mabanja awiri osowa ndikatundu ogonera.

Gulu la Tilerane la m’mudzi wa mfumu Mani M’boma la Likoma lathandiza mabanja awiri osowa ndikatundu ogonera.

by Oliver Malibisa
0 comments

Polankhula loweluka pamwambo opeleka katundu kumabanjawa, Wapampando wa Guluri mayi Gladies Njakale ati cholinga chaguluri ndikuonetsetsa kuti anthu akukhala moyo wopanda nkhawa, iwo atinso kuonjezera pakatundu yemwe apeleka lero gulu lawo lipitiliza kugwira ntchito zachifundozi.

Mayi Janet Boma azaka 62 am’mudzi wa mfumu Chilongola mdera la Khuyu omwe apindula ndi thandizori ayamikira gulu la Tilerane chifukwa chathandizoli, ndipo ati ngati nkotheka gululi likachitirenso ena.

Nawo mayi Edina Pitala azaka 83 a m’mudzi wa mfumu Mwase ayamikila gululi ndipo ati thandizoli labwela munthawi yake pomwe tili munyengo yozizira.

Gululi lapeleka bulangete, matres, komanso pilo kwawina aliyense kumabanja awiriwa

LikomaFM, OnlineNews.

You may also like

Leave a Comment

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00