Home Lifestyle Mwiniwake wa malo ogona alendo omwe akuwatcha kuti Mwayi Wanga Guest House m’boma la Likoma ati malowa awatsegulira pa 12 mwezi uno.

Mwiniwake wa malo ogona alendo omwe akuwatcha kuti Mwayi Wanga Guest House m’boma la Likoma ati malowa awatsegulira pa 12 mwezi uno.

by Chiletso Bisweck
0 comments

A Yamikani Mwambafula awuza Likoma Radio kuti pakadali pano chilichonse chokonzekera mwambowu chilimchimake ndipo ati patsikuli anthu ayembekezere kudzasangalatsidwa ndi oyimba osiyanasiyana kuphatikizapo Gibo Piason.

A Mwambafula awonjezera kuti Guest House yi ili ndizipinda zokwana 39 komanso ma charlets 10.

“Ndapanga izi podziwa kuti chilumba cha Likoma ndimbali imodzi yamalo okopela alendo m’dziko lino ndipo ndinaona kut ndithandizile kuchepetsa vuto lamalo ogona alendo”.

Iwo atinso nthawi zina alendo akabwera ochuluka ku Likoma amasowa malo ogona kaamba kakuchepa kwamalo ndipo ati ndichiyembekezo chawo kuti Mwayi Wanga Guest House ichepetsa vutoli.

Malowa omwe amangidwa mwamakono ali ndimalo wodyela komanso malo omwe makasitomala awo adzitha kumaonela mpira ndizina kudzera pa DSTV.

LikomaFM, OnlineNews.

You may also like

Leave a Comment

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00