Home FeaturedFeatured Sitima ya MV Chilembwe idziyenda kawiri patsiku kuyambila pa 15 April pakati pa boma la Likoma ndi Nkhata Bay.

Sitima ya MV Chilembwe idziyenda kawiri patsiku kuyambila pa 15 April pakati pa boma la Likoma ndi Nkhata Bay.

by Oliver Malibisa
0 comments

“Ndiyankha pompano zokhudza MV Chilembwe zomwe phungu wanyumba ya malamulo wapempha”, nduna yowona za mayendedwe ndi mtengatenga a Jacob Hara ndiwo anena izi pamwambo wotonthoza mabanja omwe akhudzidwa ndi ngozi yabwato yomwe yachitika pa 12 April m’boma la Likoma.

Ndunayi yalamula izi kutsatira pempho la phungu wadelari a Christopher Ashems Songwe.

You may also like

Leave a Comment

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00