“Ndiyankha pompano zokhudza MV Chilembwe zomwe phungu wanyumba ya malamulo wapempha”, nduna yowona za mayendedwe ndi mtengatenga a Jacob Hara ndiwo anena izi pamwambo wotonthoza mabanja omwe akhudzidwa ndi ngozi yabwato yomwe yachitika pa 12 April m’boma la Likoma.
Ndunayi yalamula izi kutsatira pempho la phungu wadelari a Christopher Ashems Songwe.