Achakwera anena izi pamsonkhano wa achinyamata omwe ukuchitikira mu mzinda wa Lilongwe pamutu wakuti ‘Harnessing Youth Innovation for Economic Employment and Sustainable Job Creation Towards Malawi 2063’, ndipo ndalama zokwana 2 billion kwacha ndizomwe zapatsidwa kwa achinyamata mu pologalamuyi.
Wapampando wabungwe la Likoma Team Adventure a Yusuf Asima omwe akuchita nawo mkumanowu akuti mkumanowu uwathandizira kwambiri kupititsa patsogolo ntchito yazokopa alendo komanso wapeleka danga pa nkhani zina zomwe achinyamata akuyenera kuchita kuti akwanilitse masomphenya a M2063.
“Kale ndinalibe uthenga okwanila pankhani ya Youth Innovation Fund koma pakadali pano ndadziwa omwe akuyenera kupindula ndi thumba limeneli”, watero Yusuf Asima.
Msonkhanowu unayamba pa 2 July ndipo udzatha pa 4 July 2025.
13 comments
https://shorturl.fm/vZQ4w
https://shorturl.fm/5yVLQ
https://shorturl.fm/0bN4x
https://shorturl.fm/mZfLn
https://shorturl.fm/NStDC
https://shorturl.fm/J0eyQ
https://shorturl.fm/3orsr
https://shorturl.fm/O61mJ
https://shorturl.fm/n8JIN
https://shorturl.fm/YMr6X
https://shorturl.fm/GlDU5
https://shorturl.fm/bGih9
https://shorturl.fm/KDjNI