Home Sports Mkulu woyendetsa nkhani za masewero m’boma la Likoma wati anthu okhala m’bomali ayembekezele kuona kusintha pa nkhani za masewero.

Mkulu woyendetsa nkhani za masewero m’boma la Likoma wati anthu okhala m’bomali ayembekezele kuona kusintha pa nkhani za masewero.

by Chiletso Bisweck
0 comments

A Antonio Manda anena izi lero pamkumano omwe amakumana ndi atsogoleri oyendetsa masewero osayinasiyana m’bomali.

M’mawu awo a Manda ati m’boma la Likoma muli zinthu zambiri zofunika kukonza pankhani za masewero, ndipo alonjeza kuti ayesetsa kusaka thandizo m’madera osiyanasiyana ndicholinga chofuna kupititsa masewera osiyanasiyana patsogolo.

“ku Likoma kuli achinyamata omwe ali ndi ma luso osiyanasiyana chomwe chikufunika nchakuti awonekele poyera,” atero a Manda.

M’modzi mwa nthumwi zomwe zinatenga nawo mbali a Raphael Malikita omwe ndi Coordinator kuchoka ku Special Olympics m’bomali ati kusowekela kwa zipangizo ndi ukadaulo wa anziphunzitsi omwe amaphunzitsa masewero osiyanasiyana nkomwe kukupangitsa kuti maluso ena asamaonekere.

Pomaliza a Manda alonjeza kuti masewera omwe atayambe ndi a Beach Soccer ndipo komiti yogwirizila inasinkhidwa kale yomwe wapampando wake ndi a Davie Kacholola.

LilkomaFM, OnlineNews.

You may also like

Leave a Comment

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

Subscribe my Newsletter for new blog posts, tips & new photos. Let's stay updated!

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00