Home Sports Mkulu woyendetsa nkhani za masewero m’boma la Likoma wati anthu okhala m’bomali ayembekezele kuona kusintha pa nkhani za masewero.

Mkulu woyendetsa nkhani za masewero m’boma la Likoma wati anthu okhala m’bomali ayembekezele kuona kusintha pa nkhani za masewero.

by Chiletso Bisweck
33 comments

A Antonio Manda anena izi lero pamkumano omwe amakumana ndi atsogoleri oyendetsa masewero osayinasiyana m’bomali.

M’mawu awo a Manda ati m’boma la Likoma muli zinthu zambiri zofunika kukonza pankhani za masewero, ndipo alonjeza kuti ayesetsa kusaka thandizo m’madera osiyanasiyana ndicholinga chofuna kupititsa masewera osiyanasiyana patsogolo.

“ku Likoma kuli achinyamata omwe ali ndi ma luso osiyanasiyana chomwe chikufunika nchakuti awonekele poyera,” atero a Manda.

M’modzi mwa nthumwi zomwe zinatenga nawo mbali a Raphael Malikita omwe ndi Coordinator kuchoka ku Special Olympics m’bomali ati kusowekela kwa zipangizo ndi ukadaulo wa anziphunzitsi omwe amaphunzitsa masewero osiyanasiyana nkomwe kukupangitsa kuti maluso ena asamaonekere.

Pomaliza a Manda alonjeza kuti masewera omwe atayambe ndi a Beach Soccer ndipo komiti yogwirizila inasinkhidwa kale yomwe wapampando wake ndi a Davie Kacholola.

LilkomaFM, OnlineNews.

You may also like

33 comments

Alanna1856 August 6, 2025 - 5:44 am Reply
Eliza554 August 6, 2025 - 6:09 am Reply
April4811 August 7, 2025 - 11:59 am Reply
Alistair4333 August 8, 2025 - 3:20 pm Reply
Annie2666 August 10, 2025 - 1:02 am Reply
Kevin107 August 10, 2025 - 2:37 am Reply
Jesse4948 August 10, 2025 - 11:48 am Reply
Harley4505 August 10, 2025 - 4:40 pm Reply
Amira3326 August 10, 2025 - 5:51 pm Reply
Lillian198 August 12, 2025 - 11:45 pm Reply
Roy3031 August 13, 2025 - 8:38 am Reply
Ana3686 August 13, 2025 - 1:13 pm Reply
Serenity1415 August 14, 2025 - 1:58 am Reply
Isaac1518 August 14, 2025 - 7:06 am Reply
Gracie4491 August 14, 2025 - 10:14 am Reply
Abram1770 August 14, 2025 - 8:16 pm Reply
Daniella1983 August 15, 2025 - 1:22 pm Reply
April1607 August 15, 2025 - 8:21 pm Reply
Freddie1943 August 15, 2025 - 11:15 pm Reply
Cassidy102 August 16, 2025 - 6:01 am Reply
Chance3956 August 16, 2025 - 6:10 am Reply
Alan4410 August 16, 2025 - 10:15 am Reply
Gwen3714 August 16, 2025 - 11:06 pm Reply
Bryan2924 August 17, 2025 - 1:04 pm Reply
Jocelyn3720 August 17, 2025 - 3:29 pm Reply
Marvin959 August 25, 2025 - 8:48 pm Reply
Ashley1055 September 5, 2025 - 12:40 am Reply
Cedric2786 September 10, 2025 - 5:16 am Reply
Alyssa3836 September 30, 2025 - 10:26 pm Reply
Ayden4347 October 9, 2025 - 8:08 am Reply
Jayla3509 November 11, 2025 - 4:30 am Reply
Lucas3180 November 13, 2025 - 9:38 am Reply
Gerard2707 December 1, 2025 - 7:12 am Reply

Leave a Reply to Ana3686 Cancel Reply

Likoma (LCR) is a community radio for Likoma District licensed by
Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) in December
2013.The Radio is covering the whole of Likoma District including
Chizumulu, parts of Nkhata Bay,Mzuzu and Nkhotakota. The radio
station enjoys a listenership of about 50,000 comprising of 17,000 from
the island and others from Nkhata Bay, Nkhotakota and some parts
of Mozambique.

Newsletter

@2025 – All Right Reserved. MACRA Community Radios

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00
Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00