A Antonio Manda anena izi lero pamkumano omwe amakumana ndi atsogoleri oyendetsa masewero osayinasiyana m’bomali.
M’mawu awo a Manda ati m’boma la Likoma muli zinthu zambiri zofunika kukonza pankhani za masewero, ndipo alonjeza kuti ayesetsa kusaka thandizo m’madera osiyanasiyana ndicholinga chofuna kupititsa masewera osiyanasiyana patsogolo.
“ku Likoma kuli achinyamata omwe ali ndi ma luso osiyanasiyana chomwe chikufunika nchakuti awonekele poyera,” atero a Manda.
M’modzi mwa nthumwi zomwe zinatenga nawo mbali a Raphael Malikita omwe ndi Coordinator kuchoka ku Special Olympics m’bomali ati kusowekela kwa zipangizo ndi ukadaulo wa anziphunzitsi omwe amaphunzitsa masewero osiyanasiyana nkomwe kukupangitsa kuti maluso ena asamaonekere.
Pomaliza a Manda alonjeza kuti masewera omwe atayambe ndi a Beach Soccer ndipo komiti yogwirizila inasinkhidwa kale yomwe wapampando wake ndi a Davie Kacholola.
LilkomaFM, OnlineNews.
33 comments
https://shorturl.fm/Yf5FB
https://shorturl.fm/kzsUN
https://shorturl.fm/vISGk
https://shorturl.fm/7Jwdb
https://shorturl.fm/ZuItY
https://shorturl.fm/qXK8x
https://shorturl.fm/ODfy4
https://shorturl.fm/4gbb7
https://shorturl.fm/oTr2V
https://shorturl.fm/l7V0J
https://shorturl.fm/WzyiJ
https://shorturl.fm/7y2oH
https://shorturl.fm/qqPfI
https://shorturl.fm/iBMuU
https://shorturl.fm/3f1XF
https://shorturl.fm/xxA9z
https://shorturl.fm/WGqVD
https://shorturl.fm/lFG7u
https://shorturl.fm/2eyQz
https://shorturl.fm/UCG3c
https://shorturl.fm/5Gpsr
https://shorturl.fm/O4zDb
https://shorturl.fm/hKoFR
https://shorturl.fm/G5XJv
https://shorturl.fm/m9RXU
https://shorturl.fm/tBCpB
https://shorturl.fm/pi1EB
https://shorturl.fm/JDTFQ
https://shorturl.fm/HvfFY
https://shorturl.fm/lZj2p
https://shorturl.fm/z7Hcd
https://shorturl.fm/isjcU
https://shorturl.fm/nZmLB