Nthambi yowona zanyengo ndi kusintha kwanyengo yati nyengo ya Chiperoni ikuyembekezeka kuchepa mphanvu lero ndipo mawa m’madera ambiri kudzakhala kwa nyengo ya dzuwa, koma mvula idzagwa m’madera ochepa am’chigawo chakumpoto.Nthambiyi ikupitiliza kuchenjeza asodzi kupewa kulowa pa nyanja pogwilitsa ntchito mabwato ang’ono ang’ono munthayi.

LikomaFM, OnlineNews.

Related posts

Sukulu ya Likoma Sekondale yalandila galimoto ya tsopano yomwe ikhale ikuchepetsa mavuto a mayendedwe.

Kuchedwetsa ntchito kwa kontilakitara kwapangitsa kuti ntchito yomanga chipatala chaching’ono cha YoMa healthy Post m’boma la Likoma chisathe munthawi yake.