Nthambi yowona zanyengo ndi kusintha kwanyengo yati nyengo ya Chiperoni ikuyembekezeka kuchepa mphanvu lero ndipo mawa m’madera ambiri kudzakhala kwa nyengo ya dzuwa, koma mvula idzagwa m’madera ochepa am’chigawo chakumpoto.Nthambiyi ikupitiliza kuchenjeza asodzi kupewa kulowa pa nyanja pogwilitsa ntchito mabwato ang’ono ang’ono munthayi.

LikomaFM, OnlineNews.

Related posts

Khonsolo ya Likoma yalandira ma Computer asanu othandizira sukulu ya Likoma community technical college kuchokera ku Bungwe la TEVETA.

Khansala Justina Phiri wa chigawo chakumpoto kwa Chilumba cha Chizumulu ndiyemwe wasankhidwa kukhala Wapampando wa Khonsolo ya Likoma.