Apolisi m’boma la Likoma amanga a Charlse Banda, powaganizira kuti anachita chipongwe msungwana wazaka khumi.
Malingana ndi mneneri wa Police ya Likoma a Andrew Kusimbwa ati kumangidwaku kwachitika pambuyo pa ntchito yomwe inachitika ndi a polisiwa. “A…