Likoma FM
  • Home
  • Featured
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Lifestyle
  • Sports
  • About Us
  • Contact
  • Login
  • Likoma FM

    Wachiwiri kwa nduna yoona za umoyo yemwenso ndi phungu wa Likoma Islands Constituency a Charles Chilambula ati kubwera kwa incinerator m’boma la Likoma kupititsa patsogolo ntchito za umoyo.

    Ofesi yowona za usodzi ku Likoma yati ndiyokondwa kuti tsopano asodzi ali ndi owaimira ku khonsolo.

    Wapampando oyang’anila chitukuko chadera la kumwera kwa chilumba cha Likoma a Anson Putaputa ati akusowekera maphunziro kuti ayambe kugwira ntchito yawo mwaukadaulo.

    Wachiwiri kwa nduna yoona za umoyo yemwenso ndi phungu wa Likoma Islands Constituency a Charles Chilambula ati kubwera kwa incinerator m’boma la Likoma kupititsa patsogolo ntchito za umoyo.

    Chiletso BisweckMarch 1, 202602 views

    A Chilambula anena izi lamulungu kutsatila kufika kwa incinerator yi pa chipatala cha Chima m’bomali. “Kumbuyoku tikafuna kuwotcha zinthu zina tinkazitumiza ku…

    Read more

    Ofesi yowona za usodzi ku Likoma yati ndiyokondwa kuti tsopano asodzi ali ndi owaimira ku khonsolo.

    Chiletso BisweckFebruary 20, 2026025 views

    Mkulu woyendetsa ntchito za usodzi m’boma la Likoma, Lonjezo Chikopa wati tsopano pakhala posavuta kuti asodzi azitha kutula nkhawa zawo komanso kudziwa…

    Read more

    Wapampando oyang’anila chitukuko chadera la kumwera kwa chilumba cha Likoma a Anson Putaputa ati akusowekera maphunziro kuti ayambe kugwira ntchito yawo mwaukadaulo.

    Chiletso BisweckFebruary 16, 2026024 views

    A Putaputa anena izi kutsatila zomwe wachiwiri kwa nduna yoona za umoyo yemwenso ndi phungu wa boma la Likoma a Charles Chilambula…

    Read more

    Wachiwiri kwa nduna ya zaumoyo yemwenso ndi phungu wa Likoma Islands Constituency olemekezeka a Charles Broomhead Chilambula ati boma ndilodzipereka kupititsa patsogolo ntchito zaumoyo.

    Chiletso BisweckFebruary 5, 2026039 views

    A Chilambula amalankhula izi lero pamwambo otsegulira chipatala chaching’ono cha YoMa chomwe chamangidwa m’mudzi wa Yofu m’boma la Likoma. A Chilambula ati…

    Read more

    Atachita zii kwa zaka zinayi m’modzi mwa oyimba wapa chilumba cha Chizumulu, Memory Pondomali yemwe amatchuka ndi dzina lakuti Nyapondo wati akhala akutulutsa nyimbo yatsopano yomwe akuyitcha “Zani”.

    Chiletso BisweckJanuary 29, 2026071 views

    Nyapondo wati nyimboyi yomwe wajambula Video komanso audio zonse zitulutsidwa pa 1 February 2026, “panopa ndikhala okhazikika chifukwa ndinawoloka zomwe zakhala zikundifowoketsa…

    Read more

    Khonsolo ya Likoma yalandira ma Computer asanu othandizira sukulu ya Likoma community technical college kuchokera ku Bungwe la TEVETA.

    Chiletso BisweckDecember 16, 20250100 views

    Polankhula lolemba pamwambo opeleka ma computer wa, mkulu woyendetsa ntchito za TEVETA m’chigawo chakumpoto a Joseph Chikopa ati ndicholinga chawo kuti Likoma…

    Read more

    Khansala Justina Phiri wa chigawo chakumpoto kwa Chilumba cha Chizumulu ndiyemwe wasankhidwa kukhala Wapampando wa Khonsolo ya Likoma.

    Chiletso BisweckNovember 10, 202513197 views

    Pa chisankho chomwe chachitika Lolemba motsogozedwa ndi bwana mkubwa wa khonsolo ya Likoma Abubakar Nkhoma, a Justina Phiri agonjetsa a Enerst Gulu…

    Read more

    Mwiniwake wa malo ogona alendo omwe akuwatcha kuti Mwayi Wanga Guest House m’boma la Likoma ati malowa awatsegulira pa 12 mwezi uno.

    Chiletso BisweckOctober 12, 20250115 views

    A Yamikani Mwambafula awuza Likoma Radio kuti pakadali pano chilichonse chokonzekera mwambowu chilimchimake ndipo ati patsikuli anthu ayembekezere kudzasangalatsidwa ndi oyimba osiyanasiyana…

    Read more

    Team ya Try Again FC yafika mu ndime yotsiliza mu chikho cha Castel Challenge Cup itagonjetsa Nkhwazi FC 2 kwa du.

    Chiletso BisweckSeptember 29, 20250126 views

    Izi zili chonchi kutsatila masewero omwe anachitika Lamulungu lapitali pa Madimba Community Ground mndime ya Semi final pakati pa Nkhwazi fc ndi…

    Read more

    ‎kutsatila kutsegulira kwa sukulu pa 22 September chaka chino, gulu la achinyamata lochokera kwa a mfumu a Mani m’mudzi wa Mbungo lapeleka makope ndi zolembera kwa ana apasukulu ya mbungo m’boma la Likoma.‎‎

    Chiletso BisweckSeptember 25, 20257244 views

    M,modzi mwa achinyamata omwe apelereka makopewa a Nick Mkuyamba ati cholinga chachikulu cha gulu lawo ndikupititsa patsogolo maphunziro musukulu za primary m’bomali.‎‎Nawo…

    Read more

    Posts navigation

    1 … 4
    View Desktop Version

    Powered by PenciDesign

    Back To Top