Khansala Justina Phiri wa chigawo chakumpoto kwa Chilumba cha Chizumulu ndiyemwe wasankhidwa kukhala Wapampando wa Khonsolo ya Likoma.

Pa chisankho chomwe chachitika Lolemba motsogozedwa ndi bwana mkubwa wa khonsolo ya Likoma Abubakar Nkhoma, a Justina Phiri agonjetsa a Enerst Gulu Banda omwe akhale wachiwiri kwa wapampando wa khonsoloyi.

Pamapeto amasankhowa a Justina alonjeza kuthandizira khonsolo ya Likoma pankhani za chitukuko powonetsetsa kuti ndondomeko zoyenera zikutsatidwa pachuma.

LikomaFM, OnlineNews.

Related posts

Mkulu woyang’anira nkhani za katemera wa Polio mdziko muno, a Blessing Nyirongo ati ali ndi chikhulupiliro kuti kampeni yopeleka katemera wamatendawa m’boma la Likoma ikhala yopambana.

Wamkulu wa kampani ya Malawi Lake Services wati kukweza mitengo kwa sitima ya MV Ilala kupititsa patsogolo ntchito za kampaniyi.

Ofesi yowona za usodzi ku Likoma yati ndiyokondwa kuti tsopano asodzi ali ndi owaimira ku khonsolo.

13 comments

Brayden4227 November 11, 2025 - 4:30 am
Eloise2533 November 12, 2025 - 4:20 pm
Alicia3983 November 13, 2025 - 9:37 am
Theo2317 November 14, 2025 - 3:03 pm
Leslie567 November 14, 2025 - 10:48 pm
Gracie1753 November 17, 2025 - 2:19 am
Gianna257 November 18, 2025 - 1:59 am
Marion3747 November 19, 2025 - 9:06 am
Pearl1465 November 23, 2025 - 1:42 am
Kane4910 November 23, 2025 - 8:27 am
Caiden4718 December 1, 2025 - 7:12 am
Conner3767 December 1, 2025 - 9:54 am
Catherine4305 December 2, 2025 - 5:52 am
Add Comment