Likoma FM
  • Home
  • Featured
  • Politics
  • Business
  • Entertainment
  • Lifestyle
  • Sports
  • About Us
  • Contact
  • Login
  • Likoma FM

    Team ya Try Again FC yafika mu ndime yotsiliza mu chikho cha Castel Challenge Cup itagonjetsa Nkhwazi FC 2 kwa du.

    ‎kutsatila kutsegulira kwa sukulu pa 22 September chaka chino, gulu la achinyamata lochokera kwa a mfumu a Mani m’mudzi wa Mbungo lapeleka makope ndi zolembera kwa ana apasukulu ya mbungo m’boma la Likoma.‎‎

    Bungwe lowona za chisankho la Malawi Electoral Commission (MEC) litsegulira nyengo ya misonkhano yokopa anthu pa 14 July 2025, pokonzekera chisankho chomwe chidzachitike pa 16 September chaka chino.

    Chiletso BisweckJuly 12, 2025096 views

    Malingana ndi kalata yomwe bungweri ladatulutsa pa 9 Julayi ndipo wasaina ndi mneneri wa bungweri a Sangwani Mwafulirwa yati mwambo otsegulira nyengo…

    Read more

    Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwela wapempha achinyamata kuti achite machawi pofusila ndalama ya mthumba la Youth Innovation Fund.

    Chiletso BisweckJuly 3, 202513167 views

    Achakwera anena izi pamsonkhano wa achinyamata omwe ukuchitikira mu mzinda wa Lilongwe pamutu wakuti ‘Harnessing Youth Innovation for Economic Employment and Sustainable…

    Read more

    Khonsolo ya Boma la Likoma yayamba ntchito yomanga nyumba yosungilamo katundu wa ngozi zogwa mwadzidzi.

    Chiletso BisweckJune 9, 20251125 views

    Ntchito yomanga nyumbayi yomwe imangidwe ku Ngani pansi pa CHAKO VDC yayambika lero ndipo igwilika kwa masiku 90. M’mawu awo nkulu oyang’anila…

    Read more

    Bishop wa Anglican Dioceses of Northern Malawi wati mpingo uli ndi udindo waukulu potengapo mbali pachitukuko chadziko lino.

    Chiletso BisweckJune 3, 20251118 views

    Rt.Rev. Fanuel Magangani wanena izi lamulungu lapitali pa St Peters Anglican Cathedral m’boma la likoma pamwambo osangalalira kuti Dioceses yi yakwanitsa zaka…

    Read more

    Phungu wa boma la Likoma a Christopher Ashems Songwe apeleka thandizo ku ofesi ya maphunziro m’bomali kuti lithandizile masewero osambila.

    Chiletso BisweckMay 31, 2025097 views

    Phunguyu wapeleka thandizo la ndalama zokwana 1,000,000.00-kwacha lachisanu kudzera ku ofesi ya za masewero, District Education Sports Officer (DESO). Polandila thandizoli mkulu…

    Read more

    Gulu la Taskforce lomwe ndi nthambi ya chipani cha Malawi Congress Party m’boma la Likoma lapeleka Cement kuti amalizile nyumba ya chigayo.

    Oliver MalibisaMay 22, 2025086 views

    Polankhula lachinayi pamwambo opeleka cement ku komiti yoyendetsa chigayochi, a Innocent Aponda omwe ndi mmodzi mwa guluri ati achita chidwi powona momwe…

    Read more

    Wapampando wa khonsolo ya boma la Likoma wati anthu omwe amapindula ndi porogalamu ya mtukula pakhomo adzigwilitsa moyenera ndalama zomwe amalandila mu porogalamuyi.

    Chiletso BisweckMay 18, 2025081 views

    A Barnabas Sambamu anena izi lamulungu pomwe khonsolo ya Likoma inakonza masewelo ampira wamiyendo ndicholinga chakuti apeleke uthenga wamomwe porogalamuyi imayendela, pamutu…

    Read more

    Gulu la Tilerane la m’mudzi wa mfumu Mani M’boma la Likoma lathandiza mabanja awiri osowa ndikatundu ogonera.

    Oliver MalibisaMay 10, 20250170 views

    Polankhula loweluka pamwambo opeleka katundu kumabanjawa, Wapampando wa Guluri mayi Gladies Njakale ati cholinga chaguluri ndikuonetsetsa kuti anthu akukhala moyo wopanda nkhawa,…

    Read more

    Pomwe dziko lino likukonzekera chisankho chapatatu bungwe loyendetsa chisankho la Malawi Electral Commission likupitiliza kudziwitsa adindo osiyanasiyana za ndondomeko yachisankho.

    Chiletso BisweckMay 10, 20250165 views

    Mkulu owona zachisankho m’boma la Likoma a Theophilus Msachi lero achititsa mkumano wa mafumu ndi atsogoleli azipembedzo pofuna kuwadziwitsa za ntchito yotsimikizila…

    Read more

    Mulandu wayemwe akumuganizira kuti ndi m’modzi mwawoyendetsa Boat lomwe linachita ngozi ndikupha anthu nkhumi ndi modzi m’mawa wapa 12 April, 2025, m’boma la Likoma wayamba lero.

    Oliver MalibisaMay 7, 20250319 views

    Malingana ndi His Worship Fordwatch Nyamazana Mkandawire wati mlanduwu ukuyembekezeka kupitilira lachisanu sabata ino. Naye otengera milandu ku bwalo lamilandu Sergeant Charles…

    Read more

    Posts navigation

    1 2 … 4
    View Desktop Version

    Powered by PenciDesign

    Back To Top